Mawu a M'munsi
b Lemba la Danieli 7:25 limanenanso za nyengo ya nthaŵi pamene ‘opatulika a Wam’mwambamwamba adzalemetsedwa.’ Monga kwafotokozedwa m’mutu wapitawo, zimenezi zinagwirizanitsidwa ndi nkhondo yoyamba ya padziko lonse.
b Lemba la Danieli 7:25 limanenanso za nyengo ya nthaŵi pamene ‘opatulika a Wam’mwambamwamba adzalemetsedwa.’ Monga kwafotokozedwa m’mutu wapitawo, zimenezi zinagwirizanitsidwa ndi nkhondo yoyamba ya padziko lonse.