Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Ngakhale kuti mngeloyu sakutchulidwa dzina, zikuoneka kuti ndi mmodzimodziyo amene mawu ake anamveka akulangiza Gabrieli kuti athandize Danieli pom’fotokozera masomphenya amene anaona. (Yerekezani Danieli 8:2, 15, 16 ndi 12:7, 8.) Ndiponso, Danieli 10:13 amasonyeza kuti Mikaeli, “wina wa akalonga omveka,” anafika kudzathandiza mngelo ameneyu. Choncho, mngelo wosatchulidwa dzina ameneyu ayenera kuti ali ndi mwayi wogwira ntchito limodzi ndi Gabrieli komanso ndi Mikaeli.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena