Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Ulosi wa pa Danieli chaputala 11 suneneratu mayina a maulamuliro andale amene amatenga malo a mfumu ya kumpoto ndi mfumu ya kumwera pa nthaŵi zosiyanasiyana. Mayinawo amadziŵika kokha pamene zochitikazo ziyamba kuoneka. Ndiponso, popeza kuti mkanganowo umachitika m’zigawozigawo, zimakhalapo nyengo zina zimene kulimbanako kumalekeka—mfumu ina imalamulira pamene inayo imangokhala.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena