Mawu a M'munsi
b Baibulo limati ‘Yehova sanali mumphepoyo, m’chivomerezicho ndiponso m’motowo.’ Atumiki a Yehova sali ngati anthu amene amalambira mphamvu zam’chilengedwe. Yehova ndi wamkulu kwambiri moti sangakwane m’chilichonse chimene analenga.—1 Mafumu 8:27.