Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Ena amaganiza kuti kale anthu ankagwiritsa ntchito chipangizo chachikale choonera zinthu zomwe zili kutali. Iwo amati, kodi anthu a nthawi imeneyo paokha akanadziwa bwanji kuti nyenyezi zilipo zambiri ndipo n’zosawerengeka? Koma amanyalanyaza mfundo yoti Yehova, yemwe ndi Mlembi wamkulu wa Baibulo, ndi amene ankathandiza anthuwo kudziwa zimenezi.​—2 Timoteyo 3:16.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena