Mawu a M'munsi
c Taganizirani kuti mungatenge nthawi yaitali bwanji kuti muwerenge nyenyezi 100 biliyoni zokha. Ngati mungakwanitse kumawerenga nyenyezi imodzi pa sekondi iliyonse, kwa maola 24 pa tsiku, mungatenge zaka 3,171 kuti mumalize kuwerenga zonsezo.