Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Nthawi zambiri panyanja ya Galileya pamatha kuyamba mphepo mwadzidzidzi. Chifukwa chakuti nyanjayi ili pamalo otsika kwambiri, mpweya wapanyanjayi umakhala wotentha kwambiri kusiyana ndi madera ozungulira. Chifukwa cha zimenezi, nyengo imakhala yosakhazikika. M’chigwa cha Yorodano mumawomba mphepo yamphamvu yochokera m’phiri la Herimoni lomwe lili kumpoto kwa nyanjayi. Nyengo yabata imatha kusintha mwadzidzidzi kenako mphepo ya mkuntho n’kuyamba.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena