Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Mawu akuti “mwana wamasiye” akusonyeza kuti Yehova amadera nkhawa kwambiri ana onse amasiye, kaya aamuna kapena aakazi. Yehova anaonetsetsa kuti m’Chilamulo mwalembedwa zokhudza chigamulo chomwe chinaperekedwa pa nkhani ya ana aakazi a Tselofekadi omwe anali amasiye. Chigamulo chimenechi chinakhala lamulo ndipo chinkateteza ufulu wa ana aakazi amasiye.​—Numeri 27:1-8.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena