Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Mu akachisi a Akanani munkakhala zipinda zapadera zoti azichitiramo zachiwerewere koma Chilamulo cha Mose chinkanena kuti anthu odetsedwa asamalowe n’komwe m’kachisi. Choncho popeza kugonana kunkachititsa munthu kukhala wodetsedwa kwa kanthawi, palibe amene mwalamulo akanachititsa kuti kugonana kukhale mbali ya kulambira panyumba ya Yehova.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena