Mawu a M'munsi
b Mawu a Chigiriki amene anawamasulira kuti “kudera nkhawa,” amatanthauza “kusokonezedwa maganizo.” Mawu a pa Mateyu 6:25 amenewa, amanena za kuda nkhawa chifukwa choopa chinachake zomwe zimachititsa kuti munthu asokonezeke maganizo komanso asamasangalale.