Mawu a M'munsi
a Mogwirizana ndi 1 Mafumu 3:16, azimayi awiriwo anali mahule. Buku la Insight on the Scriptures limati: “N’kutheka kuti azimayiwa sanali oyendayenda, koma anali mahule m’njira yakuti ankachita zachiwerewere. Mwina anali Ayuda kapenanso sanali Ayuda.”—Lofalitsidwa ndi Mboni za Yehova.