Mawu a M'munsi
b Mawu a Chigiriki amene anawamasulira kuti “ukakhazikitse mtendere,” amatanthauza “kusiya kukhala adani n’kukhala mabwenzi, kugwirizananso ndiponso kuyambiranso kuchitira zinthu limodzi.” Choncho cholinga chanu n’kuthandiza m’bale wanu amene wakhumudwayo kuti ngati zingatheke asiye kukhumudwa nanu.—Aroma 12:18.