Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Mobwerezabwereza Baibulo limasonyeza kuti pali kugwirizana pakati pa chiyembekezo choti akufa adzauka ndi zimene Yehova amakumbukira. Munthu wokhulupirikayo Yobu anauza Yehova kuti: “Zikanakhala bwino mukanandiikira nthawi n’kudzandikumbukira.” (Yobu 14:13) Yesu anatchula za kuukitsidwa kwa “onse amene ali m’manda achikumbutso.” Izi zinali zoyenera chifukwa Yehova amawakumbukira bwino kwambiri akufa amene akufuna kudzawaukitsa.​—Yohane 5:28, 29.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena