Mawu a M'munsi
a Komabe, ngakhale kuti chikondi “chimakhulupirira zinthu zonse,” sizikutanthauza kuti tizilola anthu ena kutinamiza. Baibulo limatichenjeza kuti: “Musamale ndi amene amagawanitsa anthu ndiponso kuchita zinthu zokhumudwitsa . . . choncho muziwapewa.”—Aroma 16:17.