Mawu a M'munsi
a Kuti mumve zambiri zokhudza dzina la Mulungu, tanthauzo lake komanso zifukwa zotichititsa kuligwiritsa ntchito polambira, onani kabuku kakuti Dzina la Mulungu Limene Lidzakhala Kosatha, ndiponso mutu woyamba m’Kabuku Kothandiza Kuphunzira Mawu a Mulungu. Timabukuti ndi tofalitsidwa ndi Mboni za Yehova.