Mawu a M'munsi
a Mfundo zina zosonyeza kuti Mikayeli ndi dzina lina la Mwana wa Mulungu zili m’buku la Samalani Ulosi wa Danieli!, tsamba 204-205, ndiponso m’buku la Chingelezi lakuti Insight on the Scriptures, Voliyumu 2, tsamba 393-394. Mabukuwa ndi ofalitsidwa ndi Mboni za Yehova.