Mawu a M'munsi
a Mneneri Yesaya komanso Ezekieli anachenjeza za tsiku la Yehova. Yesaya anakhala ndi moyo pa nthawi imodzi ndi aneneri ngati Hoseya ndi Mika ndipo Ezekieli anakhala ndi moyo pa nthawi imodzi ndi aneneri ngati Habakuku ndi Obadiya.—Yesaya 13:6, 9; Ezekieli 7:19; 13:5; werengani ndime 4 mpaka 6, m’Mutu 2 wa buku lino.