Mawu a M'munsi
b Kuti mupeze umboni wina wotsimikizira kuti anthu oopa Mulungu zinthu zidzawayendera bwino pa tsiku la Yehova, werengani Hoseya 6:1; Yoweli 2:32; Obadiya 17; Nahumu 1:15; Habakuku 3:18, 19; Zefaniya 2:2, 3; Hagai 2:7; Zekariya 12:8, 9; ndiponso Malaki 4:2.