Mawu a M'munsi
a Pali mafanizo atatu osangalatsa kwambiri amene angatithandize kumvetsa mfundo yakuti Yehova amakondabe kwambiri anthu ake amene anasochera. Mafanizowa ndi a nkhosa yosochera, ndalama yotayika ndiponso mwana wolowerera.—Luka 15:2-32.