Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Mawu a Chigiriki amene anawamasulira kuti “chitsanzo,” kwenikweni amatanthauza “pepala lokhala ndi zilembo limene linkaikidwa pansi pa pepala lina limene ankafuna kulembapo.” Pa anthu onse amene anauziridwa kulemba Malemba a Chigiriki, mtumwi Petulo yekha ndi amene anagwiritsa ntchito mawu amenewa ndipo anthu ena amanena kuti mawuwa amatanthauza “‘pepala lokhala ndi zilembo’ limene mwana amene akuphunzira kulemba ankaika pansi pa pepala lina kuti azilemba motsatira zilembozo ndipo amayesetsa kuti zifanane ndendende.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena