Mawu a M'munsi
b Kulalikira kumatanthauza kufalitsa kapena kulengeza uthenga. Tanthauzo la kuphunzitsa ndi lofananako ndi kulalikira, koma kuphunzitsa kumafuna zambiri monga kufotokoza zinthu mozamirapo ndiponso mwatsatanetsatane. Mphunzitsi wabwino amaphunzitsa mogwira mtima n’cholinga choti wophunzirayo achite zimene waphunzirazo.