Mawu a M'munsi
a Josephus, Mfarisi wolemba mbiri wa m’nthawi ya atumwi, amenenso ukwati wake unatha, ananena kuti kuthetsa ukwati kunali kololeka “pa chifukwa chilichonse (ndipo amuna ambiri amanena kuti ali ndi zifukwa zambiri zothetsera maukwati awo).”