Mawu a M'munsi
b Yesu ananenanso kuti wansembe ndi Mleviyo ‘ankachokera ku Yerusalemu,’ zimene zikusonyeza kuti ankachokera kukachisi. Choncho palibe amene angawaikire kumbuyo ponena kuti iwo anapewa kukhudza wovulalayo chifukwa ankaoneka ngati wafa, ndipo akanakhala osayenerera kutumikira pakachisi kwa kanthawi.—Levitiko 21:1; Numeri 19:16.