Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Pa tsiku limeneli, anthu analavulira Yesu kawiri konse. Koyamba, atsogoleri a chipembedzo ndi amene anamulavulira ndipo kachiwiri, asilikali achiroma. (Mateyu 26:59-68; 27:27-30) Ngakhale kuti Yesu ananyozedwa mwanjira imeneyi, anapirira mosanyinyirika ngakhale pang’ono. Anachita zonsezi pokwaniritsa ulosi wakuti: “Sindinabise nkhope yanga kuti asaichitire zinthu zochititsa manyazi komanso kuti asailavulire.”​—Yesaya 50:6.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena