Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

d Pangano la Chilamulo linanena kuti mkazi akabereka mwana azipereka nsembe ya machimo kwa Mulungu. (Levitiko 12:1-8) Lamulo limeneli linkawakumbutsa Aisiraeli kuti makolo amapatsira ana awo uchimo, komanso kuti aziona kubadwa kwa mwana moyenerera, ndipo liyenera kuti linawathandiza kupewa kutengera miyambo yachikunja yokhudza masiku obadwa.—Salimo 51:5.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena