Mawu a M'munsi
d Pangano la Chilamulo linanena kuti mkazi akabereka mwana azipereka nsembe ya machimo kwa Mulungu. (Levitiko 12:1-8) Lamulo limeneli linkawakumbutsa Aisiraeli kuti makolo amapatsira ana awo uchimo, komanso kuti aziona kubadwa kwa mwana moyenerera, ndipo liyenera kuti linawathandiza kupewa kutengera miyambo yachikunja yokhudza masiku obadwa.—Salimo 51:5.