Mawu a M'munsi
a Buku lina linanena kuti mawu Achigiriki amene anamasuliridwa kuti “mmisiri wa matabwa,” “amatanthauza ntchito zosiyanasiyana zimene mmisiriyo angagwire, kaya kukhoma denga la nyumba, kupanga katundu wa m’nyumba kapenanso china chilichonse chamatabwa.”