Mawu a M'munsi
d Zikuoneka kuti mu 33 C.E., ku Yerusalemu kunali Afarisi okwana 6,000 okha ndi Asaduki ochepa kwambiri. Zimenezi zingasonyeze chifukwa china chimene magulu awiriwa ankachitira mantha kwambiri ndi zimene ophunzirawo ankaphunzitsa zokhudza Yesu.