Mawu a M'munsi
b Mawu a Sitefano ali ndi mfundo zimene sizipezeka pena paliponse m’Baibulo. Mwachitsanzo iye anafotokoza kuti Mose anaphunzira nzeru za Aiguputo, anatchula zaka zimene anali nazo pamene ankathawa ku Iguputo komanso kutalika kwa nthawi imene anakhala ku Midiyani.