Mawu a M'munsi
c N’zokayikitsa ngati Khoti Lalikulu la Ayuda linkaloledwa ndi Aroma kupereka chigamulo choti munthu aphedwe. (Yoh. 18:31) Choncho zikuoneka kuti khotili silinalamule kuti Sitefano aphedwe, koma anachita kuphedwa ndi gulu la anthu amene anali atakwiya kwambiri.