Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Nthawi zambiri atumwi ndi amene anali ndi udindo wopereka mphatso ya mzimu woyera kwa anthu ena. Koma pa nthawiyi, zikuoneka kuti Yesu anapatsa Hananiya mphamvu zopereka mphatso ya mzimu kwa Saulo. Saulo atakhala wokhulupirira, panapita nthawi yaitali ndithu asanakumane ndi atumwi 12 aja. Komabe, n’kutheka kuti pa nthawi yonseyi iye ankalalikira mwakhama. Choncho Yesu anaonetsetsa kuti Saulo ali ndi mphamvu zimene zingamuthandize kugwira ntchito yolalikira imene anam’patsa.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena