Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Ayuda ena ankadana ndi anthu ofufuta zikopa chifukwa ntchitoyi inkawachititsa kuti azigwira zikopa, nyama zakufa komanso ankagwiritsa ntchito zinthu zina zonyansa pogwira ntchitoyi. Anthu ofufuta zikopa ankaonedwa kuti ndi osayenera kufika pakachisi, ndipo malo awo ogwirira ntchito ankafunika kukhala kunja kwa mzinda pa mtunda pafupifupi mamita 20. Mwina chimenechi chinali chimodzi mwa zifukwa zimene zinachititsa kuti nyumba ya Simoni ikhale “m’mbali mwa nyanja.”​—Mac. 10:6.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena