Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Dokotala wina amenenso amalemba mabuku, analemba kuti zizindikiro za matenda amene Herode ankadwala, zimene Josephus ndi Luka anafotokoza, ziyenera kuti zinayamba chifukwa cha njoka za m’mimba zimene zinadzaza m’matumbo mwake. Nthawi zina munthu amatha kusanza njoka za m’mimbazo, kapena zimatuluka m’thupi lake munthuyo akafa. Buku lina linati: “Zimene Luka anafotokoza mwatsatanetsatane monga dokotala zokhudza imfa ya [Herode], zikusonyeza kuti imfayi inali yochititsa mantha.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena