Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Paulo ankafuna kuti amusungebe Onesimo, koma kuchita zimenezi kukanakhala kuphwanya malamulo a Aroma komanso kukanakhala kumuphwanyira ufulu Filimoni, amene anali Mkhristu komanso mbuye wake wa Onesimo. Choncho Onesimo anabwerera kwa Filimoni, atatenga kalata yochokera kwa Paulo. M’kalatayo, Paulo analimbikitsa Filimoni kuti amulandire bwino Onesimo kapolo wake, amene tsopano analinso m’bale wake wauzimu.​—Filim. 13-19.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena