Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Anthu ena amaganiza kuti Yeremiya anauzidwa kupita pafupi osati kumtsinje wa Firate. N’chifukwa chiyani amaganiza choncho? Katswiri wina wa Baibulo ananena kuti: “Chifukwa chachikulu chimene anthu amatsutsira zimenezi n’choti amaganiza kuti Mulungu sakanapempha mneneriyu kuti ayende maulendo awiri ataliatali omwe atchulidwawa, kuchokera ku Yerusalemu kupita kumtsinje wa Firate.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena