Mawu a M'munsi
b Anthu ena amaganiza kuti Yeremiya anauzidwa kupita pafupi osati kumtsinje wa Firate. N’chifukwa chiyani amaganiza choncho? Katswiri wina wa Baibulo ananena kuti: “Chifukwa chachikulu chimene anthu amatsutsira zimenezi n’choti amaganiza kuti Mulungu sakanapempha mneneriyu kuti ayende maulendo awiri ataliatali omwe atchulidwawa, kuchokera ku Yerusalemu kupita kumtsinje wa Firate.”