Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Apa Yehova ankalankhula ndi anthu a mu ufumu wakumpoto wa Isiraeli wa mafuko 10. Pamene Yeremiya ankapereka uthengawu n’kuti anthu amenewa atakhala mu ukapolo kudziko la eni kwa zaka pafupifupi 100. Ndipo Yeremiya anasonyeza kuti pofika m’nthawi yake, mtunduwo unali usanalapebe. (2 Maf. 17:16-18, 24, 34, 35) Komabe, munthu aliyense payekha akanatha kubwerera kwa Mulungu ngakhalenso kubwerera kudziko lakwawo kuchoka ku ukapolo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena