Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Yesaya ananena ulosi wopita kwa anthu omwe sakanatha kukwatira m’masiku ake, amenenso sankaloledwa kuchita nawo zinthu zina polambira Mulungu m’nthawi ya Aisiraeli. Iye analosera kuti ngati anthuwo angapitirize kukhalabe omvera, adzapatsidwa zinthu “zabwino kuposa ana aamuna ndi aakazi,” zomwe ndi “dzina limene silidzatha mpaka kalekale” m’nyumba ya Mulungu.—Yes. 56:4, 5.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena