Mawu a M'munsi
a Zimene Hoseya anachitira Gomeri zinachitira bwino chithunzi mfundo yakuti Mulungu ali ndi mtima wofunitsitsa kukhululukira anthu. Onani Nsanja ya Olonda ya November 15, 2005, tsamba 17 mpaka 21, komanso onani ndemanga za lemba la Hoseya 2:14-16, m’buku lachingelezi lakuti Live With Jehovah’s Day in Mind, tsamba 128 mpaka 130.