Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Pulofesa Shapiro sakhulupirira kuti zamoyo zinachita kulengedwa. Amakhulupirira kuti zamoyo zinangokhalako mwangozi m’njira inayake yomwe panopa sitikuidziwa bwinobwino. Mu 2009, asayansi a pa yunivesite ya Manchester ku England ananena kuti anakwanitsa kupanga mamolekyu enaake otchedwa manyukiliyotaidi. Komabe, Shapiro ananena kuti zinthu zimene anagwiritsa ntchito popanga mamolekyu amenewa sizikugwirizana ndi zinthu zimene iyeyo akudziwa kuti zimapanga RNA.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena