Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Tikamanena za kuseweretsa maliseche sitikutanthauza kukhala ndi chilakolako chofuna kugonana kumene kumatha kuchitika mwachibadwa komanso mosayembekezereka. Mwachitsanzo, nthawi zina mnyamata akhoza kudzuka m’mawa zitamusokonekera polota. Atsikana enanso chilakolako chikhoza kuwapeza mosayembekezereka, makamaka akatsala pang’ono kuyamba kusamba kapena akangomaliza kumene. Tikamanena za kuseweretsa maliseche tikutanthauza kuchita zinthu mwadala zomwe zingakupangitse kumva ngati ukugonana ndi munthu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena