Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a N’zochititsa chidwi kuti Rute sanangotchula kuti “Mulungu” ngati mmene anthu amene sankalambira Yehova ankachitira. M’malomwake iye anagwiritsa ntchito dzina lenileni la Mulungu lakuti Yehova. Baibulo lina linanena kuti: “Pamenepa amene analemba buku la Rute anatsindika mfundo yoti, ngakhale kuti Rute sanali Mwisiraeli, ankalambira Mulungu woona.”—The Interpreter’s Bible.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena