Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

b Nthawi zambiri phiri la Karimeli limakhala lobiriwira komanso kumawomba kamphepo kayeziyezi kochokera m’nyanja. Zimenezi zimachititsa kuti kuzigwa mvula kawirikawiri komanso kuzikhala mame ambiri. Anthu olambira Baala ayenera kuti ankaona kuti phiri limeneli ndi malo ofunika kwambiri, chifukwa ankakhulupirira kuti Baala ndi amene amabweretsa mvula. Koma pa nthawiyi zinasonyezeratu kuti Baala ndi mulungu wonyenga chifukwa phiri la Karimeli linali litauma ndiponso linali lopanda zomera.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena