Mawu a M'munsi
b Kuti mudziwe zambiri zimene zinachitika pa zaka zimenezi komanso m’zaka zotsatira, werengani buku la Jehovah’s Witnesses—Proclaimers of God’s Kingdom, masamba 425 mpaka 520, amene akufotokoza zimene zakhala zikuchitika pa ntchito yokololayi kuyambira m’chaka cha 1919 mpaka chaka cha 1992.