Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Ayuda ochokera m’madera ena ankafunika kugwiritsa ntchito ndalama zovomerezeka popereka msonkho wapachaka wapakachisi ndipo anthu osintha ndalama ankawalipiritsa akafuna kusintha ndalama zawo kuti apeze ndalama zovomerezekazo. Anthu a m’madera enawa ankafunikanso kugula nyama zoti apereke nsembe. Yesu anatchula amalondawa kuti ndi “achifwamba,” ndipo n’kutheka kuti anawatchula choncho chifukwa choti ankalipiritsa anthu mitengo yokwera kwambiri.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena