Mawu a M'munsi
a Mu 2013, anthu ongodzipereka oposa 230,000 anavomerezedwa kuti azithandiza makomiti omanga a chigawo okwana 132 a ku United States. Chaka chilichonse makomiti a m’dzikoli ankayang’anira ntchito yomanga Nyumba za Ufumu pafupifupi 75 komanso kuthandiza kukonzanso Nyumba za Ufumu pafupifupi 900.