Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a N’zomveka kunena kuti kuwonongedwa kwa “Babulo Wamkulu” kwenikweni kukutanthauza kuwonongedwa kwa mabungwe a chipembedzo, osati kuphedwa kwa anthu onse omwe ali m’chipembedzo chonyenga. Choncho, anthu ambiri amene poyamba anali m’Babulo Wamkulu adzapulumuka kuwonongedwa kumeneku ndipo n’kutheka kuti adzayamba kulankhula zosonyeza kuti asiya zachipembedzo ngati mmene lemba la Zekariya 13:4-6 limafotokozera.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena