Mawu a M'munsi
d Pofotokoza za mawu a Chiheberi amene anawamasulira kuti “mpaka kalekale,” buku lina linati: “Kuwonjezera pa kunena za nthawi, mawuwa amatanthauzanso kuti chinthucho ndi chokhalitsa, chosatha, sichingadetsedwe, sichingachotsedwe komanso sichingasinthe.”