Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Ayuda ambiri amene anali ku ukapolo ankakhala m’midzi imene inali kutali ndi mzinda wa Babulo. Mwachitsanzo, Ezekieli ankakhala limodzi ndi Ayuda amene ankakhala pafupi ndi mtsinje wa Kebara. (Ezek. 3:15) Koma panalinso Ayuda ena ochepa amene ankakhala mumzinda. Pa gulu la anthu amenewa panali “amʼbanja lachifumu komanso anthu olemekezeka.”​—Dan. 1:3, 6; 2 Maf. 24:15.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena