Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Kuwonjezera pamenepo, Ayuda omwe anali ku ukapolo omwe ankakumbukira mmene dziko lawo linalili, ankadziwa kuti mtsinje umenewu sungakhale weniweni. Tikutero chifukwa chakuti mtsinjewu ukuyambira m’kachisi amene ali pamwamba pa phiri lalitali lomwe pamalo amene akufotokozedwawa panalibe. Komanso masomphenyawa angatanthauze kuti mtsinjewu unkalowera ku Nyanja Yakufa ndipo panalibe cholepheretsa chilichonse. Koma malinga ndi mmene dzikolo linalili zimenezinso zinali zosatheka.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena