Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO

Mawu a M'munsi

a Yehova amafunitsitsa kuthandiza anthu amtima wosweka. (Salimo 34:18) Anthu oterewa amakhala ndi ululu waukulu mumtima mwawo moti amafuna kudzipha. Koma Yehova amawamvetsa ndipo amafunitsitsa kuwathandiza. Kuti muone mmene malangizo a m’Baibulo angathandizire munthu kuti asiye kuganiza zofuna kudzipha, werengani nkhani yakuti, “Kodi Baibulo Lingandithandize Ngati Ndili ndi Maganizo Ofuna Kudzipha?” pagawo lakuti Onani Zinanso m’phunziroli.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena