Mawu a M'munsi
b Anthu amene anachotsapo mimba sayenera kumadziimba mlandu kwambiri chifukwa Yehova akhoza kuwakhululukira. Kuti mudziwe zambiri, werengani nkhani yakuti, “Kodi Baibulo Limanena Zotani pa Nkhani Yochotsa Mimba?” pagawo lakuti Onani Zinanso m’phunziroli.